Department of Climate Change and Meteorological Services
Department of Climate Change and Meteorological Services
May 15, 2025 at 02:52 PM
#zbsnews Anthu atatu akuti akusowa bwato lomwe anakwera litagudubuzika pa nyanja ya Chilwa dzulo masana. Malinga ndi zomwe tapeza bwatolo lomwe linali ndi anthu 8 komanso matumba a mpunga oposa 80 akuti lagudubuzika pafupi ndi doko la Lungazi m'boma la Zomba. M'neneri wa Polisi mchigawo chaku m'mawa a Patrick Mussa, apempha nthawi asanayankhulepo pa nkhaniyi. (by Raphael Mlozoa-Zomba:05/15/2025) #malawismostfollowedpage
😢 ❤️ 😮 🙏 29

Comments