Department of Climate Change and Meteorological Services
                                
                            
                            
                    
                                
                                
                                May 15, 2025 at 02:52 PM
                               
                            
                        
                            #zbsnews
Anthu atatu akuti akusowa bwato lomwe anakwera litagudubuzika pa nyanja ya Chilwa dzulo  masana.
Malinga ndi zomwe tapeza bwatolo lomwe linali ndi anthu 8 komanso matumba a mpunga oposa 80 akuti lagudubuzika pafupi ndi doko la Lungazi m'boma la Zomba.
M'neneri wa Polisi mchigawo chaku m'mawa a Patrick Mussa, apempha nthawi asanayankhulepo pa nkhaniyi.
(by Raphael Mlozoa-Zomba:05/15/2025)
#malawismostfollowedpage
                        
                    
                    
                    
                    
                    
                                    
                                        
                                            😢
                                        
                                    
                                        
                                            ❤️
                                        
                                    
                                        
                                            😮
                                        
                                    
                                        
                                            🙏
                                        
                                    
                                    
                                        29